Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 12:4 - Buku Lopatulika

4 pa khomo lakunja padzatsekeka; potsika mau akupera, wina nanyamuka polira mbalame, ndipo akazi onse akuimba sadzamveka bwino;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 pa khomo lakunja padzatsekeka; potsika mau akupera, wina nanyamuka polira mbalame, ndipo akazi onse akuimba sadzamveka bwino;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Makutu ako adzatsekeka ndipo sudzamva phokoso lakunja. Sudzamvanso kusinja kwapamtondo kapena kulira kwa mbalame m'mamaŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Makutu ako adzatsekeka, ndipo sudzamva phokoso lakunja; sudzamvanso kusinja kwa pa mtondo kapena kulira kwa mbalame mmawa.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 12:4
5 Mawu Ofanana  

Lero ndili nazo zaka makumi asanu ndi atatu; kodi ndikhoza kuzindikiranso kusiyanitsa zabwino ndi zoipa? Mnyamata wanu ndikhoza kodi kuzindikira chimene ndidya kapena kumwa? Kodi ndikhozanso kumva mau a amuna ndi akazi oimba? Chifukwa ninji tsono mnyamata wanu ndidzakhalanso wolemetsa mbuye wanga mfumu.


Adzatsegula ndani zitseko za pakamwa pake? Mano ake aopsa pozungulira pao.


Tenga mipero, nupere ufa; chotsa chophimba chako, vula chofunda, kwinda m'mwendo, oloka mitsinje.


Ndiponso ndidzawachotsera mau akusekera ndi mau akukondwera, ndi mau a mkwati, ndi mau a mkwatibwi, mau a mphero, ndi kuwala kwa nyali.


Ndipo mau a anthu oimba zeze, ndi a oimba, ndi a oliza zitoliro, ndi a oomba malipenga sadzamvekanso konse mwa iwe; ndipo mmisiri aliyense wa machitidwe ali onse sadzapezedwanso konse mwa iwe; ndi mau a mphero sadzamvekanso konse mwa iwe;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa