Mlaliki 12:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti Mulungu adzanena mlandu wa zochita zonse, ndi zobisika zonse, ngakhale zabwino ngakhale zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti Mulungu adzanena mlandu wa zochita zonse, ndi zobisika zonse, ngakhale zabwino ngakhale zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pajatu Mulungu adzaweruza zonse zimene timachita, zabwino kapena zoipa, ngakhale ndi zam'chinsinsi zomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pakuti Mulungu adzaweruza zochita zonse, kuphatikizanso zinthu zonse zobisika, kaya zabwino kapena zoyipa. Onani mutuwo |