Mlaliki 12:12 - Buku Lopatulika12 Pamodzi ndi izi, mwananga, tachenjezedwa; pakuti saleka kulemba mabuku ambiri; ndipo kuphunzira kwambiri kutopetsa thupi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pamodzi ndi izi, mwananga, tachenjezedwa; pakuti saleka kulemba mabuku ambiri; ndipo kuphunzira kwambiri kutopetsa thupi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Mwana wanga, uchenjere ndi kalikonse kobzola pamenepa. Kulemba mabuku sikutha, ndipo kuphunzira kwambiri kumatopetsa thupi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Samalira mwana wanga, za kuwonjezera chilichonse pa zimenezi. Kulemba mabuku ambiri sikutha, ndipo kuphunzira kwambiri kumatopetsa thupi. Onani mutuwo |