Mlaliki 11:8 - Buku Lopatulika8 Inde, munthu akakhala ndi moyo zaka zambiri, akondwere ndi zonsezo; koma akumbukire masiku amdima kuti adzachuluka. Zonse zilinkudza zili zachabe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Inde, munthu akakhala ndi moyo zaka zambiri, akondwere ndi zonsezo; koma akumbukire masiku amdima kuti adzachuluka. Zonse zilinkudza zili zachabe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Munthu akakhala wa zaka zambiri, mlekeni akondwerere zaka zonsezo. Koma azikumbukira kuti masiku otsatira imfa yake ndi ochuluka koposa. Zonse zikudzazi nzopanda phindu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Munthu akakhala wa zaka zambiri, mulekeni akondwerere zaka zonsezo, koma iye azikumbukira masiku a mdima, pakuti adzakhala ochuluka. Chilichonse chimene chikubwera ndi chopanda phindu. Onani mutuwo |