Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 11:7 - Buku Lopatulika

7 Indetu kuunika nkokoma, maso napeza bwino m'kuona dzuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Indetu kuunika nkokoma, maso napeza bwino m'kuona dzuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Kuŵala kwam'maŵa kumasangalatsa, ndipo maso ako akaona dzuŵa amakondwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Kuwala nʼkwabwino, ndipo maso amasangalala kuona dzuwa.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 11:7
10 Mawu Ofanana  

Koma anandiombola ndingatsikire kumanda, ndi moyo wanga udzaona kuunika.


kumbweza angalowe kumanda, kuti kuunika kwa moyo kumuwalire.


Pakuti mwalanditsa moyo wanga kuimfa, simunatero nao mapazi anga kuti ndingagwe? Kuti ndiyende pamaso pa Mulungu m'kuunika kwa amoyo.


Pakuti Yehova Mulungu ndiye dzuwa ndi chikopa; Yehova adzapatsa chifundo ndi ulemerero; sadzakaniza chokoma iwo akuyenda angwiro.


Kuunika kwa maso kukondweretsa mtima; ndipo pomveka zabwino mafupa amatenga uwisi.


Waumphawi ndi wotsendereza akumana; Yehova apenyetsa maso a onse awiriwo.


ngakhale lisanade dzuwa, ndi kuunika, ndi mwezi, ndi nyenyezi, mitambo ndi kubweranso italeka mvula;


Ngakhale dzuwa siliona ngakhale kulidziwa, imeneyi ipambana winayo kupuma;


Nzeru ili yabwino pamodzi ndi cholowa; akuona dzuwa apindula nayo.


kotero kuti mukakhale ana a Atate wanu wa Kumwamba; chifukwa Iye amakwezera dzuwa lake pa oipa ndi pa abwino, namavumbitsira mvula pa olungama ndi pa osalungama.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa