Mlaliki 11:7 - Buku Lopatulika7 Indetu kuunika nkokoma, maso napeza bwino m'kuona dzuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Indetu kuunika nkokoma, maso napeza bwino m'kuona dzuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Kuŵala kwam'maŵa kumasangalatsa, ndipo maso ako akaona dzuŵa amakondwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Kuwala nʼkwabwino, ndipo maso amasangalala kuona dzuwa. Onani mutuwo |