Mlaliki 10:18 - Buku Lopatulika18 Tsindwi litewa ndi mphwai za eni ake; nyumba nidontha ndi ulesi wa manja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Tsindwi litewa ndi mphwai za eni ake; nyumba nidontha ndi ulesi wa manja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Denga limaloshoka, mwini wake akakhala waulesi, ndipo nyumba imadontha, mwiniwake akakhala nthyamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ngati munthu ndi waulesi, denga lake limaloshoka; ngati manja ake ndi alobodo nyumba yake imadontha. Onani mutuwo |