Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mlaliki 1:15 - Buku Lopatulika

15 Chokhotakhota sichingaongokenso; ndipo choperewera sichingawerengedwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Chokhotakhota sichingaongokenso; ndipo choperewera sichingawerengedwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Chimene chidakhota sichingathe kuwongokanso, chimene palibe sichingathe kuŵerengedwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Chinthu chokhota sichingathe kuwongoledwa; chimene palibe sichingathe kuwerengedwa.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 1:15
10 Mawu Ofanana  

nakufotokozere zinsinsi za nzeru, popeza zipindikapindika machitidwe ao! Chifukwa chake dziwa kuti Mulungu akuiwalira mphulupulu zina.


Iye akapatsa mpumulo adzamtsutsa ndani? Akabisa nkhope yake adzampenyerera ndani? Chikachitika pa mtundu wa anthu, kapena pa munthu, nchimodzimodzi;


Ndidziwa kuti zonse Mulungu azichita zidzakhala kufikira nthawi zonse; sungaonjezepo kanthu, ngakhale kuchotsapo; Mulungu nazichita kuti anthu akaope pamaso pake.


Ndinapotoka ndi mtima wanga womwe kudziwa ndi kusanthula ndi kufunafuna nzeru ndi malongosoledwe a zinthu, ndi kudziwa kuti udyo ndiwo utsiru, ndi kuti kupusa ndi misala;


Chigwa chilichonse chidzadzazidwa, ndipo phiri lililonse ndi chitunda chilichonse zidzachepetsedwa, ndipo zokhota zidzaongoledwa, ndipo zamakolokoto zidzasalala;


Kodi angathe Mkusi kusanduliza khungu lake, kapena nyalugwe mawanga ake? Pamenepo mungathe inunso kuchita zabwino, inu amene muzolowera kuchita zoipa.


Ndani anganene, chonena chake ndi kuchitikadi, ngati Ambuye salamulira?


ndi okhala padziko lapansi onse ayesedwa achabe; ndipo Iye achita mwa chifuniro chake m'khamu la kumwamba ndi mwa okhala padziko lapansi; ndipo palibe woletsa dzanja lake, kapena wakunena naye, Muchitanji?


Ndipo ndani wa inu ndi kudera nkhawa angathe kuonjezera pa msinkhu wake mkono umodzi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa