Mlaliki 1:14 - Buku Lopatulika14 Ndaona ntchito zonse zipangidwa kunja kuno; ndipo zonsezo ndi chabe ndi kungosautsa mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndaona ntchito zonse zipangidwa kunja kuno; ndipo zonsezo ndi chabe ndi kungosautsa mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Zonse zochitika pansi pano ndaziwona. Zonsezo nzopandapake, ndipo kuzifunafuna nkungodzivuta chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ine ndaona zinthu zonse zochitika pansi pano; zinthu zonsezo ndi zopandapake, nʼkungodzivuta chabe. Onani mutuwo |