Miyambo 9:3 - Buku Lopatulika3 Yatuma anamwali ake, iitana pa misanje ya m'mudzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Yatuma anamwali ake, iitana pa misanje ya m'mudzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Idatuma adzakazi ake kuti akakhalire pa malo apamwamba mu mzinda ndipo akalengeze kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Nzeruyo inatuma adzakazi ake, kuti akakhale pamwamba penipeni pa mzinda ndi kukalengeza kuti, Onani mutuwo |