Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 8:3 - Buku Lopatulika

3 pambali pa chipata polowera m'mudzi, polowa anthu pa makomo ifuula:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 pambali pa chipata polowera m'mudzi, polowa anthu pa makomo ifuula:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Imafuula pafupi ndi zipata kumaso kwa mzinda, ndiponso pamakomo poloŵera, imati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Imafuwula pafupi ndi zipata zolowera mu mzinda, pa makomo olowera imafuwula kuti,

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 8:3
7 Mawu Ofanana  

Muja ndinatuluka kunka kuchipata kumzinda, muja ndinakonza pokhala panga kukhwalala,


iitana posonkhana anthu polowera pachipata; m'mzinda inena mau ake,


Ndinu ndikuitanani, amuna, mau anga ndilankhula kwa ana a anthu.


Chifukwa chake pitani inu kumphambano za njira, ndipo aliyense amene mukampeze, itanani kuukwatiku.


Yesu anayankha iye, Ine ndalankhula zomveka kwa dziko lapansi; ndinaphunzitsa Ine nthawi zonse m'sunagoge ndi mu Kachisi, kumene amasonkhana Ayuda onse; ndipo mobisika sindinalankhule kanthu.


Pitani, ndipo imirirani, nimulankhule mu Kachisi kwa anthu onse mau a Moyo umene.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa