Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 8:2 - Buku Lopatulika

2 Iima pamwamba pa mtunda, pa mphambano za makwalala;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Iima pamwamba pa mtunda, pa mphambano za makwalala;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Nzeru imakhala pa zitunda m'mbali mwa njira, imakaima pa mphambano za miseu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Nzeru imayima pa zitunda mʼmbali mwa njira, imayima pa mphambano ya misewu.

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 8:2
2 Mawu Ofanana  

Ukhala pa khomo la nyumba yake, pampando pa misanje ya m'mudzi,


Yatuma anamwali ake, iitana pa misanje ya m'mudzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa