Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 7:4 - Buku Lopatulika

4 Nena kwa nzeru, Ndiwe mlongo wanga; nutche luntha mbale wako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Nena kwa nzeru, Ndiwe mlongo wanga; nutche luntha mbale wako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Nzeru uiwuze kuti, “Iwe ndiwe mlongo wanga,” ndipo khalidwe la kumvetsa zinthu ulitchule kuti, “Bwenzi langa lapamtima.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Nzeru uyiwuze kuti, “Iwe ndiwe mlongo wanga,” ndipo khalidwe lomvetsa bwino zinthu ulitchule kuti, “Bwenzi langa lapamtima.”

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 7:4
8 Mawu Ofanana  

Ndikati kwa dzenje, Ndiwe atate wanga; kwa mphutsi, Ndiwe mai wanga ndi mlongo wanga;


Uwamange pa zala zako, uwalembe pamtima pako.


Kuti zikutchinjirizire kwa mkazi wachiwerewere, kwa mlendo wamkazi wosyasyalika ndi mau ake.


Mwenzi utakhala ngati mlongo wanga, woyamwa pa bere la amai! Ndikadakupeza panja, ndikadakupsompsona; osandinyoza munthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa