Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 7:3 - Buku Lopatulika

3 Uwamange pa zala zako, uwalembe pamtima pako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Uwamange pa zala zako, uwalembe pamtima pako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Achite ngati waŵamangirira ku chala, ngati waŵadinda mumtima mwako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Uchite ngati wawamangirira pa zala zako, ndiponso ngati kuti wawalemba pa mtima pako.

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 7:3
11 Mawu Ofanana  

Chifundo ndi choonadi zisakusiye; uzimange pakhosi pako; uzilembe pamtima pako;


Asachoke kumaso ako; uwasunge m'kati mwa mtima wako.


uwamange pamtima pako osaleka; uwalunze pakhosi pako.


Nena kwa nzeru, Ndiwe mlongo wanga; nutche luntha mbale wako.


Tsopano pita, ukalembe mauwa pamaso pao pathabwa, nuwalembe m'buku, kuti akakhalebe kunthawi yam'tsogolo, mboni ya masiku onse.


Ndipo kunena za Ine, ili ndi pangano langa ndi iwo, ati Yehova; mzimu wanga umene uli pa iwe, ndi mau anga amene ndaika m'kamwa mwako sadzachoka m'kamwa mwako, pena m'kamwa mwa ana ako, pena m'kamwa mwa mbeu ya mbeu yako, ati Yehova, kuyambira tsopano ndi kunthawi zonse.


Tchimo la Yuda lalembedwa ndi peni lachitsulo, ndi nsonga ya diamondi; lalembedwa pa cholembapo cha m'mtima mwao, ndi pa nyanga za maguwa a nsembe ao.


Koma ili ndi pangano limene ndidzapangana ndi nyumba ya Israele atapita masiku aja, ati Yehova; ndidzaika chilamulo changa m'kati mwao, ndipo m'mtima mwao ndidzachilemba; ndipo ndidzakhala Mulungu wao, nadzakhala iwo anthu anga;


popeza mwaonetsedwa kuti muli kalata ya Khristu, wakumtumikira ndi ife, wosalembedwa ndi kapezi iai, koma ndi Mzimu wa Mulungu wamoyo; wosati m'magome amiyala, koma m'magome a mitima yathupi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa