Miyambo 7:2 - Buku Lopatulika2 Sunga malangizo anga, nukhale ndi moyo; ndi malamulo anga ngati mwana wa diso lako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Sunga malangizo anga, nukhale ndi moyo; ndi malamulo anga ngati mwana wa diso lako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Utsate malamulo anga, ndipo udzakhala ndi moyo. Usamale malangizo anga monga umachitira ndi maso ako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Utsate malamulo anga ndipo udzakhala ndi moyo; samala malangizo angawa monga uchitira ndi maso ako. Onani mutuwo |