Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 7:18 - Buku Lopatulika

18 Tiye tikondwere ndi chikondano mpaka mamawa; tidzisangalatse ndi chiyanjano.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Tiye tikondwere ndi chikondano mpaka mamawa; tidzisangalatse ndi chiyanjano.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Bwera tsono, tikhale malo amodzi mpaka m'maŵa, tisangalatsane ndi chikondi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Bwera, tiye tikhale malo amodzi kukondwerera chikondi mpaka mmawa; tiye tisangalatsane mwachikondi!

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 7:18
5 Mawu Ofanana  

Usachite chigololo.


ndakapiza pamphasa panga mankhwala onunkhira a mure ndi chisiyo ndi sinamoni.


Pakuti mwamuna kulibe kwathu, wapita ulendo wa kutali;


madzi akuba atsekemera, ndi chakudya chobisika chikoma.


ndi munthu akagona naye, koma kumbisikira maso a mwamuna wake, ndi kumng'unira; nadetsedwa mkaziyo, koma palibe mboni yomtsutsa, kapena sanamgwire alimkuchita;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa