Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 6:8 - Buku Lopatulika

8 koma zitengeratu zakudya zao m'malimwe; ndipo zituta dzinthu zao m'masika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 koma zitengeratu zakudya zao m'malimwe; nizituta dzinthu zao m'masika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Komabe imakonzeratu chakudya chake m'malimwe, ndipo imatuta chakudyacho m'masika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 komabe zimasungiratu chakudya chake nthawi ya chilimwe ndipo zimatuta chakudyacho nthawi yokolola.

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 6:8
5 Mawu Ofanana  

Wokolola m'malimwe ndi mwana wanzeru; koma wogona pakututa ndi mwana wochititsa manyazi.


mkaka wa mbuzi udzakukwanira kudya; ndi a pa banja lako ndi adzakazi ako.


Nyerere ndi mtundu wosalimba, koma zitengeratu zakudya zao m'malimwe.


Udzagona mpaka liti, waulesi iwe? Udzauka kutulo tako liti?


nadzikundikire okha maziko okoma ku nyengo ikudzayi, kuti akagwire moyo weniweniwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa