Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 6:3 - Buku Lopatulika

3 Chita ichi tsono; mwananga, nudzipulumutse; popeza walowa m'dzanja la mnzako, pita nudzichepetse, numdandaulire mnzako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Chita ichi tsono; mwananga, nudzipulumutse; popeza walowa m'dzanja la mnzako, pita nudzichepetse, numdandaulire mnzako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Ndiye iwe mwana wanga, popeza kuti wadziponya m'manja mwa mnzako, chita izi kuti udzipulumutse: nyamuka, pita msanga, ukampemphe kuti akumasule.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Tsono popeza iwe mwana wanga wadziponya mʼmanja mwa mnansi wako, chita izi kuti udzipulumutse: pita msanga ukamupemphe mnansi wako; kuti akumasule!

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 6:3
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide ananena ndi Gadi, Ndipsinjika mtima kwambiri, tigwe m'dzanja la Yehova; pakuti zifundo zake nzazikulu; koma tisagwe m'dzanja la munthu.


Pamenepo Semaya mneneri anadza kwa Rehobowamu, ndi kwa akalonga a Yuda, atasonkhana ku Yerusalemu chifukwa cha Sisake, nati nao, Atero Yehova, Inu mwandisiya Ine, chifukwa chake Inenso ndasiya inu m'dzanja la Sisake.


nachita choipa pamaso pa Yehova Mulungu wake; sanadzichepetse kwa Yeremiya mneneri wakunena zochokera pakamwa pa Yehova.


Ndipo simunandipereke m'dzanja la mdani; munapondetsa mapazi anga pali malo.


Ndipo Mose ndi Aroni analowa kwa Farao nanena naye, Atero Yehova, Mulungu wa Ahebri, Ukana kudzichepetsa pamaso panga kufikira liti? Lola anthu anga amuke, akanditumikire;


wakodwa ndi mau a m'kamwa mwako, wagwidwa ndi mau a m'kamwa mwako.


Usaone tulo m'maso mwako, ngakhale kuodzera zikope zako.


Dzichepetseni pamaso pa Ambuye, ndipo adzakukwezani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa