Miyambo 5:4 - Buku Lopatulika4 Chimaliziro chake nchowawa ngati chivumulo, ndi chakuthwa ngati lupanga lakuthawa konsekonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Chimaliziro chake nchowawa ngati chivumulo, ndi chakuthwa ngati lupanga lakuthawa konsekonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma kotsiriza kwake ngwoŵaŵa ngati chivumulo, ngwolasa ngati lupanga lakuthwa konsekonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 koma kotsirizira kwake ngowawa ngati ndulu; ngakuthwa ngati lupanga lakuthwa konsekonse. Onani mutuwo |