Miyambo 5:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti milomo ya mkazi wachiwerewere ikukha uchi; m'kamwa mwake muti see koposa mafuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti milomo ya mkazi wachiwerewere ikukha uchi; m'kamwa mwake muti see koposa mafuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Paja mkazi wadama ali ndi pakamwa pokoma ngati uchi, mau ake ndi osalala koposa mafuta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pakuti mkazi wachigololo ali ndi mawu okoma ngati uchi. Zoyankhula zake ndi zosalala ngati mafuta, Onani mutuwo |