Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 5:16 - Buku Lopatulika

16 Kodi magwero ako ayenera kumwazika kunja, ndi mitsinje ya madzi m'makwalala?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Kodi magwero ako ayenera kumwazika kunja, ndi mitsinje ya madzi m'makwalala?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Kodi ana ako azingoti mbwee ponseponse ngati madzi ongoyenda m'miseu?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Kodi akasupe ako azingosefukira mʼmisewu? Kodi mitsinje yako izingoyendayenda mʼzipata za mzinda?

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 5:16
13 Mawu Ofanana  

Ndipo anamdalitsa Rebeka, nati kwa iye, Mlongo wathu ndiwe, iwe ukhale amai wa anthu zikwizikwi, mbeu zako zigonjetse chipata cha iwo akudana nao.


Taonani, ana ndiwo cholowa cha kwa Yehova; chipatso cha m'mimba ndicho mphotho yake.


Mkazi wako adzanga mpesa wopatsa m'mbali za nyumba yako; ana ako adzanga timitengo ta azitona pozinga podyera pako.


Lemekezani Mulungu m'misonkhano, ndiye Yehova, inu a gwero la Israele.


Imwa madzi a m'chitsime mwako, ndi madzi oyenda a m'kasupe mwako.


Ikhale ya iwe wekha, si ya alendo okhala nawe ai.


Adalitsike kasupe wako; ukondwere ndi mkazi wokula nayo.


madzi akuba atsekemera, ndi chakudya chobisika chikoma.


Mlongo wanga, mkwatibwi ndiye munda wotsekedwa; ngati kasupe wotsekedwa, ndi chitsime chopikiza.


Ndiwe kasupe wa m'minda, chitsime cha madzi amoyo, ndi mitsinje yoyenda yochokera ku Lebanoni.


Ndipo iwo sanamve ludzu, pamene Iye anawatsogolera m'mapululu; anawatulutsira madzi kutuluka m'matanthwe; anadulanso thanthwe, madzi nabulika.


Ndipo Israele akhala mokhazikika pa yekha; kasupe wa Yakobo; akhala m'dziko la tirigu ndi vinyo; inde thambo lake likukha mame.


Ndipo anali nao ana aamuna makumi atatu; ndi ana aakazi makumi atatu anawakwatitsa kwina, natengera ana ake aamuna ana aakazi makumi atatu ochokera kwina. Ndipo anaweruza Israele zaka zisanu ndi ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa