Miyambo 5:16 - Buku Lopatulika16 Kodi magwero ako ayenera kumwazika kunja, ndi mitsinje ya madzi m'makwalala? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Kodi magwero ako ayenera kumwazika kunja, ndi mitsinje ya madzi m'makwalala? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Kodi ana ako azingoti mbwee ponseponse ngati madzi ongoyenda m'miseu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kodi akasupe ako azingosefukira mʼmisewu? Kodi mitsinje yako izingoyendayenda mʼzipata za mzinda? Onani mutuwo |