Miyambo 5:10 - Buku Lopatulika10 kuti mphamvu yako isakhutitse alendo, ndi kuti usagwire ntchito m'nyumba ya wachilendo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 kuti mphamvu yako isakhutitse alendo, ndi kuti usagwire ntchito m'nyumba ya wachilendo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mwinanso alendo adzadyerera chuma chako, phindu la ntchito zako lidzagwa m'manja mwa munthu wachilendo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 kapenanso alendo angadyerere chuma chako ndi phindu la ntchito yako kulemeretsa anthu ena. Onani mutuwo |