Miyambo 4:4 - Buku Lopatulika4 Atate nandiphunzitsa, nati kwa ine, mtima wako uumirire mau anga; sunga malamulo anga, nukhale ndi moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Atate nandiphunzitsa, nati kwa ine, mtima wako uumirire mau anga; sunga malamulo anga, nukhale ndi moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 atatewo adandiphunzitsa ndi mau akuti, “Ugwiritse mumtima mwako zimene ndikukuuzazi, usunge malamulo anga, kuti ukhale ndi moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndipo abambo anandiphunzitsa ndi mawu akuti, “Ugwiritse mawu anga pa mtima pako, usunge malamulo anga kuti ukhale ndi moyo. Onani mutuwo |