Miyambo 4:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti ndinali mwana kwa atate wanga, wokondedwa ndi mai, ndine ndekha, sanabale wina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti ndinali mwana kwa atate wanga, wokondedwa ndi mai, ndine ndekha, sanabale wina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pamene ndinali mwana m'nyumba mwa atate anga, m'menemo ndili kamwana kapamtima ka amai anga, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Paja ndinalinso mwana mʼnyumba mwa abambo anga; mwana mmodzi yekha wapamtima pa amayi anga. Onani mutuwo |