Miyambo 4:2 - Buku Lopatulika2 pakuti ndikuphunzitsani zabwino; musasiye chilangizo changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 pakuti ndikuphunzitsani zabwino; musasiye chilangizo changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ine ndikukupatsani malamulo abwino, musasiye zimene ndikukuphunzitsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Zimene ndikukuphunzitsani ndi zabwino. Choncho musasiye malangizo anga. Onani mutuwo |