Miyambo 4:1 - Buku Lopatulika1 Ananu, mverani mwambo wa atate, nimutchere makutu mukadziwe luntha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ananu, mverani mwambo wa atate, nimutchere makutu mukadziwe luntha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ana inu, mverani malangizo a atate anu, tcherani khutu, kuti mupate nzeru zodziŵira zinthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ananu, mverani malangizo a abambo anu; tcherani khutu kuti mupeze nzeru zodziwira zinthu. Onani mutuwo |