Miyambo 3:3 - Buku Lopatulika3 Chifundo ndi choonadi zisakusiye; uzimange pakhosi pako; uzilembe pamtima pako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chifundo ndi choonadi zisakusiye; uzimange pakhosi pako; uzilembe pamtima pako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Khalidwe la kudzipereka ndi kukhulupirika zisakuthaŵe, makhalidwe ameneŵa uziyenda nawo ngati mkanda wam'khosi, uŵalembe mumtima mwako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Makhalidwe ochitira ena chifundo ndi owonetsa kukhulupirika asakuchokere. Uwamangirire mʼkhosi mwako ngati mkanda ndi kuwalemba pa mtima pako. Onani mutuwo |