Miyambo 3:2 - Buku Lopatulika2 pakuti adzakuonjezera masiku ambiri, ndi zaka za moyo ndi mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 pakuti adzakuonjezera masiku ambiri, ndi zaka za moyo ndi mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ukatero zaka za moyo wako zidzachuluka, ndipo udzakhala ndi moyo wabwino kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ukatero zaka za moyo wako zidzachuluka ndipo udzakhala pa mtendere. Onani mutuwo |