Miyambo 3:1 - Buku Lopatulika1 Mwananga, usaiwale malamulo anga, mtima wako usunge malangizo anga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mwananga, usaiwale malamulo anga, mtima wako usunge malangizo anga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mwana wanga, usaiŵale malangizo angaŵa, koma mtima wako usunge malamulo anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mwana wanga, usayiwale malangizo anga, mtima wako usunge malamulo anga. Onani mutuwo |