Miyambo 26:2 - Buku Lopatulika2 Monga mpheta ilikuzungulira, ndi namzeze alikuuluka, momwemo temberero la pachabe silifikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Monga mpheta ilikuzungulira, ndi namzeze alikuuluka, momwemo temberero la pachabe silifikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Monga imachitira mpheta yokhalira kuuluka, monga amachitira namzeze kumangoti zwezwezwe, ndimonso limachitira temberero lopanda chifukwa, silitha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ngati timba wokhalira kuwuluka kapena namzeze wokhalira kuzungulirazungulira, ndi mmenenso limachitira temberero lopanda chifukwa, silichitika. Onani mutuwo |