Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 26:18 - Buku Lopatulika

18 Monga woyaluka woponya nsakali, mivi, ndi imfa,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Monga woyaluka woponya nsakali, mivi, ndi imfa,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Monga munthu wopenga amene amangoponya nsakali zamoto, kapena mivi yoopsa,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Monga munthu wamisala amene akuponya sakali zamoto kapena mivi yoopsa,

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 26:18
5 Mawu Ofanana  

Eni uta anavutitsa iye kwambiri, namponyera iye, namzunza.


Wochitira mnzake umboni wonama ndiye chibonga, ndi lupanga, ndi muvi wakuthwa.


mpaka muvi ukapyoza mphafa yake; amtsata monga mbalame yothamangira msampha; osadziwa kuti adzaononga moyo wake.


Taonani, inu nonse amene muyatsa moto, amene mudzimangira m'chuuno ndi nsakali, yendani inu m'chilangali cha moto wanu, ndi pakati pa nsakali zimene mwaziyatsa. Ichi mudzakhala nacho cha padzanja langa; mudzagona pansi ndi chisoni.


Namuka Samisoni, nagwira ankhandwe mazana atatu, natenga miuni, nalunza michira, naika muuni pakati pa michira iwiri iliyonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa