Miyambo 24:4 - Buku Lopatulika4 Kudziwa kudzaza zipinda zake ndi chuma chonse chofunika cha mtengo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Kudziwa kudzaza zipinda zake ndi chuma chonse chofunika cha mtengo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Wodziŵa zinthu angathe kudzaza zipinda zake ndi chuma chokondweretsa ndi cha mtengo wapatali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Munthu wodziwa zinthu angathe kudzaza zipinda zake ndi chuma chamtengowapatali ndiponso chabwino. Onani mutuwo |