Miyambo 2:4 - Buku Lopatulika4 ukaifunafuna ngati siliva, ndi kuipwaira ngati chuma chobisika; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ukaifunafuna ngati siliva, ndi kuipwaira ngati chuma chobisika; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Uziifunafuna nzeruyo ngati siliva, ndi kumaiwunguza ngati chuma chobisika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 ngati ufunafuna nzeruyo ngati siliva ndi kuyisakasaka ngati chuma chobisika, Onani mutuwo |