Miyambo 2:3 - Buku Lopatulika3 ukaitananso luntha, ndi kufuulira kuti ukazindikire; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ukaitananso luntha, ndi kufuulira kuti ukazindikire; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndikutitu upemphe mtima wozindikira zinthu, ndi kupemba kuti ukhale womvetsa zinthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 ngati upempha kuti uzindikire zinthu inde kupempha ndi mtima wonse kuti ukhale womvetsa zinthu, Onani mutuwo |