Miyambo 2:2 - Buku Lopatulika2 kutcherera makutu ako kunzeru, kulozetsa mtima wako kukuzindikira; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 kutcherera makutu ako kunzeru, kulozetsa mtima wako kukuzindikira; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Uzitchera khutu ku nzeru, uziikapo mtima pa kumvetsa zinthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ndiponso kutchera khutu lako ku nzeru ndi kuyikapo mtima pa kumvetsa zinthu; Onani mutuwo |