Miyambo 2:1 - Buku Lopatulika1 Mwananga, ukalandira mau anga, ndi kusunga malamulo anga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mwananga, ukalandira mau anga, ndi kusunga malamulo anga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mwana wanga, uvomere mau anga, ndi kusunga bwino malamulo anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mwana wanga, ngati ulandira mawu anga ndi kusunga malamulo anga mu mtima mwako, Onani mutuwo |