Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 2:1 - Buku Lopatulika

1 Mwananga, ukalandira mau anga, ndi kusunga malamulo anga;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Mwananga, ukalandira mau anga, ndi kusunga malamulo anga;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mwana wanga, uvomere mau anga, ndi kusunga bwino malamulo anga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mwana wanga, ngati ulandira mawu anga ndi kusunga malamulo anga mu mtima mwako,

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 2:1
21 Mawu Ofanana  

Sindinabwerera kusiya malamulo a pa milomo yake; ndasungitsa mau a pakamwa pake koposa lamulo langalanga.


Mutidziwitse kuwerenga masiku athu motero, kuti tikhale nao mtima wanzeru.


kulandira mwambo wakusamalira machitidwe, chilungamo, chiweruzo ndi zolunjika;


Wosunga chilamulo ndiye mwana wozindikira; koma mnzao wa adyera achititsa atate wake manyazi.


Mwananga, usaiwale malamulo anga, mtima wako usunge malangizo anga;


Ananu, mverani mwambo wa atate, nimutchere makutu mukadziwe luntha;


Tamvera mwananga, nulandire mau anga; ndipo zaka za moyo wako zidzachuluka.


uwamange pamtima pako osaleka; uwalunze pakhosi pako.


Mwananga, sunga mau anga, ukundike malangizo anga,


Kodi nzeru siitana, luntha ndi kukweza mau ake?


Nzeru yamanga nyumba yake, yasema zoimiritsa zake zisanu ndi ziwiri;


Ufumu wa Kumwamba uli wofanana ndi chuma chobisika m'munda; chimene munthu anachipeza, nachibisa; ndipo m'kuchikonda kwake achoka, nagulitsa zonse ali nazo, nagula munda umenewu.


Koma Maria anasunga mau awa onse, nawalingalira mumtima mwake.


Ndipo anatsika nao pamodzi nadza ku Nazarete; nawamvera iwo: ndipo amake anasunga zinthu izi zonse mumtima mwake.


Alowe mau amenewa m'makutu anu; pakuti Mwana wa Munthu adzaperekedwa m'manja a anthu.


Ndipo silikhala tsidya la nyanja, kuti mukati, Adzatiolokera ndani tsidya la nyanja, ndi kutitengera ili, ndi kutimvetsa ili, kuti tilichite?


Mauwa ali okhulupirika ndi oyenera konse kuti awalandire, kuti Khristu Yesu anadza kudziko lapansi kupulumutsa ochimwa; wa iwowa ine ndine woposa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa