Miyambo 17:3 - Buku Lopatulika3 Siliva ali ndi mbiya yosungunulira, golide ali ndi ng'anjo; koma Yehova ayesa mitima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Siliva ali ndi mbiya yosungunulira, golide ali ndi ng'anjo; koma Yehova ayesa mitima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Siliva amamuyesera m'chitofu, golide amamuyesera m'ng'anjo, koma mitima amaiyesa ndi Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Siliva amamuyesa mʼngʼanjo ndipo golide amamuyesa mʼngʼanjo, koma Yehova amayesa mitima. Onani mutuwo |