Miyambo 13:2 - Buku Lopatulika2 Munthu adzadya zabwino ndi zipatso za m'kamwa mwake; koma moyo wa achiwembu udzadya chiwawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Munthu adzadya zabwino ndi zipatso za m'kamwa mwake; koma moyo wa achiwembu udzadya chiwawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Munthu wabwino amapeza nako phindu kulankhula kwake, koma anthu onyenga amalakalaka zandeu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Munthu amapeza zinthu zabwino chifukwa cha mawu ake, koma anthu osakhulupirika amalakalaka zachiwawa basi. Onani mutuwo |