Miyambo 11:3 - Buku Lopatulika3 Kuongoka mtima kwa olungama kuwatsogolera; koma kukhota kwa achiwembu kudzawaononga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Kuongoka mtima kwa olungama kuwatsogolera; koma kukhota kwa achiwembu kudzawaononga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ungwiro wa anthu olungama umaŵatsogolera, koma makhalidwe okhota a anthu onyenga ngoononga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ungwiro wa anthu olungama umawatsogolera, koma anthu osakhulupirika amawonongeka ndi chinyengo chawo. Onani mutuwo |