Miyambo 11:10 - Buku Lopatulika10 Olungama akapeza bwino, mzinda usekera; nufuula pakuonongeka oipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Olungama akapeza bwino, mudzi usekera; nufuula pakuonongeka oipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mulungu akamadalitsa anthu ake, mzinda wonse umatukuka. Oipa akaonongeka, anthu amafuula mwachimwemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Anthu olungama zinthu zikamawayendera bwino, mzinda wonse umakondwera, ndipo oyipa akamawonongeka anthu amafuwula mwachimwemwe. Onani mutuwo |
napenya, ndi kuona mfumu inaima pa nsanamira yake polowera; ndi atsogoleri, ndi malipenga, anali kwa mfumu; ndi anthu onse a m'dziko anakondwera, naomba amalipenga; oimbira omwe analiko ndi zoimbirazo, nalangiza poimbira cholemekeza. Pamenepo Ataliya anang'amba zovala zake, nati, Chiwembu, chiwembu.