Miyambo 10:3 - Buku Lopatulika3 Yehova samvetsa njala moyo wa wolungama; koma amainga chifuniro cha wochimwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Yehova samvetsa njala moyo wa wolungama; koma amainga chifuniro cha wochimwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chauta salola kuti munthu womukondweretsa iye, azikhala ndi njala, koma zimene woipa amazilakalaka, Mulungu amam'mana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Yehova salola kuti munthu wolungama azikhala ndi njala; koma amalepheretsa zokhumba za anthu oyipa. Onani mutuwo |