Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 10:2 - Buku Lopatulika

2 Chuma cha uchimo sichithangata; koma chilungamo chipulumutsa kuimfa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Chuma cha uchimo sichithangata; koma chilungamo chipulumutsa kuimfa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Chuma chochipeza monyenga sichipindulitsa, koma chilungamo chimapulumutsa ku imfa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Chuma chochipeza mwachinyengo sichipindulitsa, koma chilungamo chimapulumutsa ku imfa.

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 10:2
15 Mawu Ofanana  

Chuma sichithandiza tsiku la mkwiyo; koma chilungamo chipulumutsa kuimfa.


M'khwalala la chilungamo muli moyo; m'njira ya mayendedwe ake mulibe imfa.


Chuma cholandiridwa mokangaza chidzachepa; koma wokundika ndi dzanja adzaona zochuluka.


Kupata chuma ndi lilime lonama ndiko nkhungu yoyendayenda, ngakhale misampha ya imfa.


Adzataya siliva wao kumakwalala, nadzayesa golide wao chinthu chodetsedwa; siliva wao ndi golide wao sadzakhoza kuwalanditsa tsiku la mkwiyo wa Yehova, sadzakwaniritsa moyo wao, kapena kudzaza matumbo ao; pakuti izi ndi chokhumudwitsa cha mphulupulu zao.


Chifukwa chake, mfumu, kupangira kwanga kukomere inu, dulani machimo anu ndi kuchita chilungamo, ndi mphulupulu zanu mwa kuchitira aumphawi chifundo; kuti kapena nthawi ya mtendere wanu italike.


Ngakhale siliva wao, ngakhale golide wao sizidzakhoza kuwalanditsa tsiku la mkwiyo wa Yehova; koma dziko lonse lidzatha ndi moto wa nsanje yake; pakuti adzachita chakutsiriza, mofulumira, onse okhala m'dziko.


Koma kolingana ndi kuuma kwako, ndi mtima wako wosalapa, ulikudziunjikira wekha mkwiyo pa tsiku la mkwiyo ndi la kuvumbulutsa kuweruza kolungama kwa Mulungu;


kuti, monga uchimo unachita ufumu muimfa, chomwechonso chisomo chikachite ufumu mwa chilungamo, kufikira moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye wathu.


ndi kupezedwa mwa Iye, wosati wakukhala nacho chilungamo changa cha m'lamulo, koma chimene cha mwa chikhulupiriro cha Khristu, chilungamocho chochokera mwa Mulungu ndi chikhulupiriro;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa