Miyambo 10:2 - Buku Lopatulika2 Chuma cha uchimo sichithangata; koma chilungamo chipulumutsa kuimfa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Chuma cha uchimo sichithangata; koma chilungamo chipulumutsa kuimfa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chuma chochipeza monyenga sichipindulitsa, koma chilungamo chimapulumutsa ku imfa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Chuma chochipeza mwachinyengo sichipindulitsa, koma chilungamo chimapulumutsa ku imfa. Onani mutuwo |