Miyambo 1:9 - Buku Lopatulika9 pakuti izi ndi korona wa chisomo pamutu pako, ndi mkanda pakhosi pako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 pakuti izi ndi korona wa chisomo pamtu pako, ndi mkanda pakhosi pako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Zili ngati nsangamutu yokongola yamaluŵa pamutu pako, zili ngati mkanda wa m'khosi mwako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ali ngati sangamutu yokongola ya maluwa pamutu pako ndiponso ali ngati mkanda mʼkhosi mwako. Onani mutuwo |