Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 1:4 - Buku Lopatulika

4 kuchenjeza achibwana, kuphunzitsa mnyamata kudziwa ndi kulingalira;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 kuchenjeza achibwana, kuphunzitsa mnyamata kudziwa ndi kulingalira;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Ngophunzitsa anthu wamba nzeru za kuchenjera, ndi achinyamata kudziŵa zinthu ndi kulingalira bwino.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ndi yothandiza munthu wamba kuti aphunzire nzeru za kuchenjera, achinyamata kudziwa zinthu bwino ndi kulingalira.

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 1:4
19 Mawu Ofanana  

Yehova asunga opusa; ndidafooka ine, koma anandipulumutsa.


Potsegulira mau anu paunikira; kuzindikiritsa opusa.


Mnyamata adzayeretsa mayendedwe ake bwanji? Akawasamalira monga mwa mau anu.


Malamulo a Yehova ali angwiro, akubwezera moyo; mboni za Yehova zili zokhazikika, zakuwapatsa opusa nzeru.


Idzani ananu ndimvereni ine, ndidzakulangizani zakumuopa Yehova.


Mwananga, zisachokere kumaso ako; sunga nzeru yeniyeni ndi kulingalira;


Ine Nzeru ndikhala m'kuchenjera, ngati m'nyumba yanga; ndimapeza kudziwa ndi zolingalira.


Akundikonda ndiwakonda; akundifunafuna adzandipeza.


Ndipo tsopano, ananga, mundimvere ine, ngodala akusunga njira zanga.


Achibwana inu, chenjerani, opusa inu, khalani ndi mtima wozindikira;


Kondwera ndi unyamata wako, mnyamata iwe; mtima wako nukasangalale masiku a unyamata wako, nuyende m'njira za mtima wako, ndi monga maso ako aona; koma dziwitsa kuti Mulungu adzanena nawe mlandu wa zonsezi.


Ndipo kudzakhala khwalala kumeneko, ndi njira, ndipo idzatchedwa njira yopatulika; odetsedwa sadzapita m'menemo; koma Iye adzakhala nao oyenda m'njira, ngakhale opusa, sadzasochera m'menemo.


Chifukwa chake asungeni, achiteni; pakuti ichi ndi nzeru zanu ndi chidziwitso chanu pamaso pa mitundu ya anthu akumva malemba ndi kuti, Ndithu mtundu waukulu uwu, ndiwo athu anzeru ndi akuzindikira.


Koma thawa zilakolako za unyamata, nutsate chilungamo, chikhulupiriro, chikondi, mtendere, pamodzi ndi iwo akuitana pa Ambuye ndi mitima yoyera.


Momwemonso anyamata uwadandaulire akhale odziletsa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa