Miyambo 1:4 - Buku Lopatulika4 kuchenjeza achibwana, kuphunzitsa mnyamata kudziwa ndi kulingalira; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 kuchenjeza achibwana, kuphunzitsa mnyamata kudziwa ndi kulingalira; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ngophunzitsa anthu wamba nzeru za kuchenjera, ndi achinyamata kudziŵa zinthu ndi kulingalira bwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndi yothandiza munthu wamba kuti aphunzire nzeru za kuchenjera, achinyamata kudziwa zinthu bwino ndi kulingalira. Onani mutuwo |