Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 1:3 - Buku Lopatulika

3 kulandira mwambo wakusamalira machitidwe, chilungamo, chiweruzo ndi zolunjika;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 kulandira mwambo wakusamalira machitidwe, chilungamo, chiweruzo ndi zolunjika;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 kuti alandire mwambo wochita zinthu mwanzeru, akhale angwiro, achilungamo ndi osakondera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 kuti alandire malangizo othandiza kuti achite zinthu mwanzeru, akhale wangwiro, wachilungamo ndiponso wosakondera.

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 1:3
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Aisraele onse anamva maweruzidwe ake idaweruza mfumu, naopa mfumu; pokhala anaona kuti nzeru ya Mulungu inali mwa iye yakuweruza.


Landira tsono chilamulo pakamwa pake, nuwasunge maneno ake mumtima mwako.


Tamvera uphungu, nulandire mwambo, kuti ukhale wanzeru pa chimaliziro chako.


kuti ukadziwitse ntheradi yake ya mau oona, nukabwere ndi mau oona kwa iwo amene anakutumiza?


Mlalikiyo anasanthula akapeze mau okondweretsa, ndi zolemba zoongoka ngakhale mau oona.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa