Miyambo 1:2 - Buku Lopatulika2 Kudziwa nzeru ndi mwambo; kuzindikira mau ozindikiritsa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Kudziwa nzeru ndi mwambo; kuzindikira mau ozindikiritsa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ngothandiza kuti anthu adziŵe nzeru ndi mwambo, kuti amvetse mau a matanthauzo ozama, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndi yothandiza kuti munthu adziwe nzeru ndi malangizo; kuti amvetse mawu a matanthauzo ozama; Onani mutuwo |