Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 1:1 - Buku Lopatulika

1 Miyambo ya Solomoni mwana wa Davide, mfumu ya Israele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Miyambo ya Solomoni mwana wa Davide, mfumu ya Israele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Aŵa ndi malangizo a Solomoni, mwana wa Davide, mfumu ya Israele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Iyi ndi miyambi ya Solomoni mwana wa Davide, mfumu ya Israeli:

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 1:1
14 Mawu Ofanana  

Tsono Solomoni anakhala pa mpando wachifumu wa Davide atate wake, ndipo ufumu wake unakhazikika kwakukulu.


Ndipo Yehova anapatsa Solomoni nzeru monga momwe adamlonjezera; ndipo panali mtendere pakati pa Hiramu ndi Solomoni, iwo awiri napangana pamodzi.


taona, udzabala mwana, ndiye adzakhala munthu wa phee; ndipo ndidzampumulitsira adani ake onse pozungulirapo, pakuti dzina lake lidzakhala Solomoni; ndipo ndidzapatsa Israele mtendere ndi bata masiku ake;


ndi mwa ana anga onse (pakuti Yehova wandipatsa ana aamuna ambiri), anasankha Solomoni mwana wanga akhale pa mpando wachifumu wa ufumu wa Yehova kuweruza Israele.


Momwemo Solomoni anakhala pa mpando wachifumu wa Yehova, ndiye mfumu m'malo mwa Davide atate wake, nalemerera, namvera iye Aisraele onse.


Nafa atakalamba bwino, wochuluka masiku, zolemera, ndi ulemerero; ndi Solomoni mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Mwana wanzeru akondweretsa atate; koma mwana wopusa amvetsa amake chisoni.


kuti ukadziwitse ntheradi yake ya mau oona, nukabwere ndi mau oona kwa iwo amene anakutumiza?


Iyinso ndiyo miyambo ya Solomoni imene anthu a Hezekiya mfumu ya Yuda anailemba.


Mau a Mlaliki, mwana wa Davide, mfumu ya mu Yerusalemu.


Ndiponso pokhala wanzeru Mlalikiyo anaphunzitsabe anthu nzeru; inde, anatchera makutu nafunafuna nalongosola miyambi yambiri.


Zinthu izi ndalankhula ndi inu m'mafanizo; ikudza nthawi imene sindidzalankhula ndi inu m'mafanizo, koma ndidzakulalikirani inu m'mafanizo, koma ndidzakulalikirani inu momveka za Atate.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa