Mateyu 27:65 - Buku Lopatulika65 Pilato anati kwa iwo, Tengani alonda; mukani, kasungeni monga mudziwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201465 Pilato anati kwa iwo, Tengani alonda; mukani, kasungeni monga mudziwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa65 Pilato adaŵauza kuti, “Paja alonda muli nawo. Pitani, kalondeni pamandapo monga mukudziŵira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero65 Pilato anayankha kuti, “Tengani mlonda kalondereni monga mudziwira.” Onani mutuwo |