Mateyu 27:63 - Buku Lopatulika63 nanena, Mfumu, takumbukira ife kuti wonyenga uja anati, pamene anali ndi moyo, Ndidzauka pofika masiku atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201463 nanena, Mfumu, takumbukira ife kuti wonyenga uja anati, pamene anali ndi moyo, Ndidzauka pofika masiku atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa63 Adamuuza kuti, “Bwana, tikukumbukira kuti munthu wonyenga uja akali moyo ankati, ‘Patapita masiku atatu, ndidzaukanso.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero63 Iwo anati, “Bwana takumbukira kuti munthu wonyenga uja akanali ndi moyo anati, ‘Pakatha masiku atatu ndidzauka.’ Onani mutuwo |