Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 27:59 - Buku Lopatulika

59 Ndipo Yosefe anatenga mtembo, naukulunga m'nsalu yabafuta yoyeretsa,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

59 Ndipo Yosefe anatenga mtembo, naukulunga m'nsalu yabafuta yoyeretsa,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

59 Tsono Yosefe adautenga, naukulunga m'nsalu yoyera yabafuta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

59 Yosefe anatenga mtembowo, nawukulunga nsalu yabafuta.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:59
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye adzaononga m'phiri limeneli chophimba nkhope chovundikira mitundu yonse ya anthu, ndi nsalu yokuta amitundu onse.


yemweyo anapita kwa Pilato, napempha mtembo wa Yesu. Pomwepo Pilato analamula kuti uperekedwe.


nauika m'manda ake atsopano, osemedwa m'mwala, nakunkhunizira mwala waukulu pakhomo pa manda, nachokapo.


Ndipo anagula bafuta, namtsitsa Iye, namkulunga m'bafutamo, namuika m'manda osemedwa m'thanthwe; nakunkhunizira mwala pakhomo la manda.


Ndipo anautsitsa, naukulunga m'nsalu yabafuta, nauika m'manda osemedwa m'mwala, m'menemo sanaike munthu ndi kale lonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa