Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 27:58 - Buku Lopatulika

58 yemweyo anapita kwa Pilato, napempha mtembo wa Yesu. Pomwepo Pilato analamula kuti uperekedwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

58 yemweyo anapita kwa Pilato, napempha mtembo wa Yesu. Pomwepo Pilato analamula kuti uperekedwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

58 Iyeyu adakapempha mtembo wa Yesu kwa Pilato. Pilato adalamula kuti ampatse mtembowo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

58 Anapita kwa Pilato kukapempha mtembo wa Yesu, ndipo Pilato analamula kuti uperekedwe kwa iye.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:58
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene panali madzulo, anadza munthu wachuma wa ku Arimatea, dzina lake Yosefe, amene analinso wophunzira wa Yesu;


Ndipo Yosefe anatenga mtembo, naukulunga m'nsalu yabafuta yoyeretsa,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa